Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Levitiko 1:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo wansembe abwere naco ku guwa la nsembe, namwetule mutu wace, naitenthe pa guwa la nsembe; ndi mwazi wace aukamulire pa mbali ya guwa la nsembe,

Werengani mutu wathunthu Levitiko 1

Onani Levitiko 1:15 nkhani