Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 8:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Kunena za nsembe za zopereka zanga, aphera nsembe yanyama, naidya; koma Yehova sazilandira; tsopano adzakumbukila mphulupulu yao, nadzalanga zocimwa zao; adzabwerera kumka ku Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 8

Onani Hoseya 8:13 nkhani