Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 7:15-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Cinkana ndawalangiza ndi kulimbitsa manja ao, andilingiririra coipa,

16. Abwerera, koma si kwa Wam'mwambayo; akunga uta wosakhulupirika; akalonga ao adzagwa ndi lupanga mwa cipongwe ca lilime lao; ici ndico adzawasekera m'dziko la Aigupto.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 7