Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 4:11-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Cigololo, ndi vinyo, ndi vinyo watsopano, zicotsa mtima,

12. Anthu anga afunsira ku mtengo wao, ndi ndodo yao iwafotokozera; pakuti mzimu wacigololo wawalakwitsa, ndipo acita cigololo kucokera Mulungu wao.

13. Pamwamba pa mapiri aphera nsembe, nafukiza pazitunda, patsinde pa thundu, ndi miniali, ndi mkundi; popeza mthunzi wace ndi wabwino, cifukwa cace ana anu akazi acita citole, ndi apongozi anu acita cigololo.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 4