Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 3:4-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Pakuti ana Israyeli adzakhala masiku ambiri a opanda mfumu, ndi opanda kalonga, ndi opanda nsembe, ndi opanda coimiritsa, ndi opanda efodi kapena aterafi;

5. atatero ana a Israyeli adzabwera, nadzafuna Yehova Mulungu wao, ndi Davide mfumu yao, nadzafika ndi mantha kwa Yehova, ndi ku ukoma wace masiku otsiriza.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 3