Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 13:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Samariya adzasanduka wabwinja, pakuti anapandukana ndi Mulungu wace; iwo adzagwa ndi lupanga, ana ao amakanda adzaphwanyika, ndi akazi ao okhala ndi pakati adzatumbulidwa.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 13

Onani Hoseya 13:16 nkhani