Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Hoseya 13:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Cinkana abala mwa abale ace, mphepo ya kum'mawa idzafika, mphepo ya Yehova yokwera kucokera kucipululu; ndi gwero lace lidzaphwa, ndi kasupe wace adzauma, adzafunkha cuma ca akatundu onse ofunika.

Werengani mutu wathunthu Hoseya 13

Onani Hoseya 13:15 nkhani