Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Habakuku 3:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Munaturukira cipulumutso ca anthu anu,Cipulumutso ca odzozedwa anu;Munakantha mutu wa nyumba yawoipa,Ndi kufukula maziko kufikira m'khosi.

Werengani mutu wathunthu Habakuku 3

Onani Habakuku 3:13 nkhani