Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Habakuku 2:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndiponso vinyo ngwonyenga, ngati munthu wodzikuza, wosakhala kwao; wakukulitsa cikhumbo cace ngati kunsi kwa manda, akunga imfa, yosakhuta, koma adzisonkhanitsira amitundu onse, nadzimemezera mitundu yonse ya anthu.

Werengani mutu wathunthu Habakuku 2

Onani Habakuku 2:5 nkhani