Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 44:11-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Ndipo anafulumira natsitsa pansi zense thumba lace, namasula yense humba lace.

12. Ndipo iye anafunauna kuyambira pa wamkuru naleka pa wamng'ono; nacipeza cikho n'thumba la Benjamini:

13. ndipo anang'amba zobvala zao, nasenzetsa yense buru wace, nabwera kumuzi.

14. Yudanso ndi abale ace anadza cu nyumba ya Yosefe; ndipo iye ikali pamenepo; ndipo anagwa oansi patsogolo pace.

15. Ndipo losefe anati kwa iwo, Ici nciani nwacicita? Kodi simudziwa kuti nunthu ngati ine ndingathe kuzindidra ndithu?

Werengani mutu wathunthu Genesis 44