Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 44:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo Yosefe anauza tsanyumba wace kuti, Dzaza matumba a anthuwo ndi cakudya, monga angathe kunyamula, ndi kuika ndalama za yense kukamwa kwa thumba lace.

2. Nuike cikho canga, cikho casiliva ciija, kukamwa kwa thumba la wamng'ono, pamodzi ndi ndalama za tirigu zace. Ndipo iye anacita monga mau ananena Yosefe.

Werengani mutu wathunthu Genesis 44