Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 42:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yosefe anaona abale ace, ndipo anazindikira iwo, koma anadziyesetsa kwa iwo ngati mlendo, nanena kwa iwo mwankhanza: ndipo anati kwa iwo, Mufuma kuti inu? nati iwo, Ku dziko la Kanani kudzagula cakudya.

Werengani mutu wathunthu Genesis 42

Onani Genesis 42:7 nkhani