Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 4:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Adamu anadziwanso mkazi wace; ndipo anabala mwana wamwamuna, namucha dzina lace Seti: Cifukwa, nati iye, Mulungu wandilowezera ine mbeu yina m'malo mwa Abele amene Kaini anamupha,

Werengani mutu wathunthu Genesis 4

Onani Genesis 4:25 nkhani