Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 36:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mibadwo ya Esau (ndiye Edomu) ndi iyi:

2. Esau anatenga akazi ace a ana akazi a m'Kanani: Ada mwana wamkazi wa Eloni Mhiti, ndi Oholibama mwana wamkazi wa Ana, mwana wamkazi wa Zibeoni Mhivi;

3. ndi Basemati mwana wamkazi wa lsmayeli, mlongo wace wa Nabayoti.

4. Ndipo Ada anambalira Esau Elifazi; ndipo Basemati anabala Reueli;

Werengani mutu wathunthu Genesis 36