Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 3:23-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Yehova Mulungu anamturutsa iye m'munda wa Edene, kuti alime nthaka m'mene anamtenga iye.

24. Ndipo anamuingitsa munthuyo; nakhazika Makerubi ca kum'mawa kwace kwa munda wa Edene, ndi lupanga lamoto lakuzungulira ponsepo, lakusunga njira ya ku mtengo wa moyo.

Werengani mutu wathunthu Genesis 3