Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 3:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati Yehova Mulungu, Taonani, munthuyo akhala ngati mmodzi wa ife, wakudziwa zabwino ndi zoipa: ndipo tsopano kuti asatambasule dzanja lace ndi kutenga za mtengo wa moyo, ndi kudya, ndi kukhala ndi moyo nthawi zonse,

Werengani mutu wathunthu Genesis 3

Onani Genesis 3:22 nkhani