Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 29:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo panali m'mamawa, anaona kuti ndi Leya; ndipo anati kwa Labani, Ciani wandicitira ine? Kodi sindinakutumikira iwe cifukwa ca Rakele? wandinyenga ine bwanji?

Werengani mutu wathunthu Genesis 29

Onani Genesis 29:25 nkhani