Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 28:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo ananka kwa Ismayeli, naonjezera kwa akazi amene anali nao, natenga Mahalati mwana wamkazi wa Ismayeli mwana wa Abrahamu, mlongo wace wa Nebayoti akhalemkazi wace.

Werengani mutu wathunthu Genesis 28

Onani Genesis 28:9 nkhani