Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 27:42 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anauza Rebeka mau a Esau mwana wace wamkuru: ndipo iye anatumiza naitana Yakobo mwana wace wamng'ono, nati kwa iye, Taona, mkuru wako Esau, kunena za iwe, adzitonthoza yekha mtima wace kuti adzakupha iwe.

Werengani mutu wathunthu Genesis 27

Onani Genesis 27:42 nkhani