Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 26:5-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. cifukwa kuti Abrahamu anamvera mau anga, nasunga cilangizo canga, ndi maweruziro anga, ndi malemba anga ndi malamulo anga.

6. Ndipo Isake anakhala m'Gerari;

7. ndipo anthu a kumeneko anamfunsa iye za mkazi wace; ndipo iye anati, diye mlongowanga: cifukwa kuti anaopa kunena, Mkazi wanga; anati, anthu a kumeneko angandiphe ine cifukwa ca Rebeka; popeza anali wokongola pakumuona.

Werengani mutu wathunthu Genesis 26