Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 26:10-13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Ndipo Abimeleke anati, Nciani cimeneci waticitira ife? panatsala pang'ono ena a anthu akadagona naye mkazi wako, ndipo ukadaticimwitsa ife:

11. Ndipo Abimeleke anauza anthu ace, nati, Ali yense amene akhudza mwamuna uyo kapena mkazi wace, zoonatu adzaphedwa.

12. Ndipo Isake anabzala m'dzikomo, nalandira za makumi khumi caka cimeneco; ndipo Yehova anamdalitsa iye.

13. Ndipo anakula munthuyo, nakulakula kufikira kuti anakhala wamkurukuru:

Werengani mutu wathunthu Genesis 26