Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 24:65 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa mnyamata, Munthuyo ndani amene ayenda m'munda kukomana ndi ife? Mnyamatayo ndipo anati, Uyo ndi mbuyanga: cifukwa cace namwali anatenga cophimba cace nadziphimba.

Werengani mutu wathunthu Genesis 24

Onani Genesis 24:65 nkhani