Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 22:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abrahamu analawira m'mamawa namanga buru wace, natengako anyamata ace awiri pamodzi naye, ndi Isake mwana wace, nawaza nkhuni za nsembe, nauka, nanka kumalo komwe Mulungu anamuuza iye,

Werengani mutu wathunthu Genesis 22

Onani Genesis 22:3 nkhani