Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 22:18-24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. m'mbeu zako mitundu yonse ya dziko lap ansi idzadalitsidwa: cifukwa wamvera mau anga.

19. Ndipo Abrahamu anabwera kwa anyamata ace, ndipo anauka nayenda pamodzi kumuka ku Beereseba; ndipo anakhala Abrahamu pa Beereseba.

20. Ndipo panali zitapita izi, anauza Abrahamu kuti, Taonani, Milika iyenso anambalira Nahori mphwako ana;

21. Huzi woyamba ndi Buzi mphwace, ndi Kemueli atate wace wa Aramu;

22. ndi Kesede, ndi Hazo, ndi Pilidasi ndi Yidilafi, ndi Betuele.

23. Ndimo Betuele anabala Rebeka: amenewa asanu ndi atatu Milika anambalira Nahori mphwace wa Abrahamu.

24. Ndipo mkazi wace wamng'ono, dzina lace Rcuma, iyenso anabala Teba, ndi Gahamu, ndi Tahasi, ndi Maaka.

Werengani mutu wathunthu Genesis 22