Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 22:12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mthenga anati, Usaike dzanja lako pa mwana, usamcitire iye kanthu; cifukwa tsopano ndidziwa kuti iwe umuopa Mulungu, pakuti sunandikanize ine mwana wako, mwana wako wayekha.

Werengani mutu wathunthu Genesis 22

Onani Genesis 22:12 nkhani