Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 17:24-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

24. Ndipo Abrahamu anali wa zaka makumi asanu ndi anai kudza zisanu ndi zinai, pamene anadulidwa m'khungu lace.

25. Ndipo Ismayeli mwana wace anali wa zaka khumi ndi zitatu pamene anadulidwa m'khungu lace.

26. Tsiku lomwelo anadulidwa Abrahamu ndi Ismayeli mwana wace.

27. Ndipo amuna onse a m'nyumba mwace obadwa m'nyumba, ndi ogulidwa ndi ndalama kwa alendo, anadulidwa pamodzi naye.

Werengani mutu wathunthu Genesis 17