Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 17:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Abrahamu adagwa nkhope pansi, naseka, nati m'mtima mwace, Kodi mwana adzabadwa kwa iye amene ali wa zaka zana? Kodi Sara wa zaka makumi asanu ndi anai adzabala?

Werengani mutu wathunthu Genesis 17

Onani Genesis 17:17 nkhani