Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 14:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anaturuka mfumu ya Sodomu, ndi ya Gomora, ndi mfumu ya Adima, ndi mfumu ya Zeboimu, ndi mfumu ya Bela (kumeneko ndi ku Zoari) ndipo anawathira nkhondo m'cigwa ca Sidimu

Werengani mutu wathunthu Genesis 14

Onani Genesis 14:8 nkhani