Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 12:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Yehova anati kwa Abramu, Turuka iwe m'dziko lako, ndi kwa abale ako, ndi ku nyumba ya atate wako, kunka ku dziko limene ndidzakusonyeza iwe;

Werengani mutu wathunthu Genesis 12

Onani Genesis 12:1 nkhani