Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Genesis 1:12-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Ndipo dziko lapansi linamera maudzu, therere lobala mbeu monga mwa mtundu wace, ndi mtengo wakubala zipatso, momwemo muli mbeu yace, monga mwa mtundu wace; ndipo anaona Mulungu kuti kunali kwabwino.

13. Ndipo panali madzulo ndipo panali m'mawa, tsiku lacitatu.

14. Ndipo Mulungu anati, Pakhale zounikira pa thambo la kumwamba, zakulekanitsa usana ndi usiku; zikhale zizindikiro ndi nyengo, ndi masiku, ndi zaka;

Werengani mutu wathunthu Genesis 1