Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 6:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pokhala inu ponse midzi idzapasuka, ndi misanje idzakhala yabwinja; kuti maguwa anu a nsembe akhale opasuka ndi mabwinja, ndi mafano anu asweke nalekeke, ndi zoimiritsa zanu zadzuwa zilikhidwe, ndi nchito zanu zifafanizidwe.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 6

Onani Ezekieli 6:6 nkhani