Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 46:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Uziperekanso kwa Yehova mwana wa nkhosa wa caka cimodzi akhale nsembe yopsereza wopanda cirema, tsiku ndi tsiku, m'mawa ndi m'mawa, uzimpereka.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 46

Onani Ezekieli 46:13 nkhani