Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 42:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo anati kwa ine, Zipinda za kumpoto, ndi zipinda za kumwela, ziri cakuno ca mpatawo, ndizo zipinda zopatulika, kumene ansembe okhala pafupi pa Yehova azidyera zinthu zopatulikitsa; kumeneko aziika zopatulikitsa, ndi nsembe yaufa, ndi nsembe yaucimo, ndi nsembe yoparamula; pakuti malowo ndi opatulika.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 42

Onani Ezekieli 42:13 nkhani