Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 4:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo Ine ndakuikira zaka za mphulupulu yao ngati masiku, ndiwo masiku mazana atatu mphambu makumi asanu ndi anai, kuti usenze mphulupulu ya nyumba ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4

Onani Ezekieli 4:5 nkhani