Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 4:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwe ugonere pansi mbali yako ya kumanzere, nuikepo mphulupulu ya nyumba ya Israyeli; monga mwa kuwerenga kwa masiku amene udzagonapo udzasenza mphulupulu yao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4

Onani Ezekieli 4:4 nkhani