Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 37:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndidzapangana nao pangano la mtendere, lidzakhala pangano losatha nao, ndipo ndidzawakhazika, ndi kuwacurukitsa, ndi kuika malo anga opatulika pakati pao kosatha.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 37

Onani Ezekieli 37:26 nkhani