Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 34:9-11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

9. cifukwa cace, abusa inu, imvani mau a Yehova:

10. Atero Ambuye Yehova, Taonani, Ine ndiipidwa nao abusa, ndidzafunsa nkhosa zanga pa dzanja lao, ndi kuwaletsa asadyetsenso nkhosazo, ngakhale kudzidyetsa okha sadzacitanso; ndipo ndidzalanditsa nkhosa zanga pakamwa pao, zisakhale cakudya cao.

11. Pakuti atero Ambuye Yehova, Taonani, Ine, Inedi ndidzapwaira nkhosa zanga ndi kuzifunafuna.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 34