Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 28:23 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndidzatumiza mliri ndi mwazi ilowe m'makwalala ace, ndi olasidwa adzagwa m'kati mwace ndi lupanga lougwera pozungulira ponse; motero adzadziwa kuti Ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 28

Onani Ezekieli 28:23 nkhani