Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 24:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ine Yehova ndacinena, cidzacitika; ndipo ndidzacicita, sindidzamasula, kapena kulekerera, kapena kuwaleka, monga mwa njira zako, ndi monga umo unacitira adzakuweruza iwe, ati Ambuye Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 24

Onani Ezekieli 24:14 nkhani