Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 23:45 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu olungama adzawaweruza monga mwa maweruzo a acigololo, ndi maweruzo a akazi okhetsa mwazi; pakuti ndiwo acigololo, ndi m'manja mwao muli mwazi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 23

Onani Ezekieli 23:45 nkhani