Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 22:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ansembe ace acitira coipa cilamulo canga, nadetsa zopatulika zanga, sasiyanitsa pakati pa zopatulika ndi zosapatulika, ndipo sazindikiritsa anthu pakati pa zodetsa ndi zoyera, nabisira masabata anga maso ao; ndipo Ine ndidetsedwa pakati pao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 22

Onani Ezekieli 22:26 nkhani