Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 22:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pali ciwembu ca aneneri ace pakati pace, ngati mkango wobangula womwetula nyama, analusira miyoyo, alanda cuma ndi za mtengo wace, acurukitsa amasiye pakati pace.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 22

Onani Ezekieli 22:25 nkhani