Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 20:43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi pomwepo mudzakumbukila njira zanu, ndi zonse mudazicita ndi kudzidetsa nazo, ndipo mudzakhala onyansa pamaso pa inu nokha, cifukwa ca zoipa zanu zonse mudazicita.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:43 nkhani