Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 17:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Panalinso ciombankhanga cina cacikuru, ndi mapiko akuru, ndi nthenga zambiri; ndipo taona, mpesa uwu unacipindira mizu yace, nucilunjikitsira nthambi zace, kucokera pookedwa pace, kuti ciuthirire madzi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 17

Onani Ezekieli 17:7 nkhani