Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 16:39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzakuperekanso m'dzanja lao, ndipo adzagwetsa nyumba yako yacimphuli, ndi kugumula ziunda zako, nadzakubvula zobvala zako, ndi kulanda zokometsera zako zokongola, nadzakusiya wamarisece ndi wausiwa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 16

Onani Ezekieli 16:39 nkhani