Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 12:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamaso pao uwasenze paphewa pako, ndi kuwaturutsa kuli mdima, nuphimbe nkhope yako kuti usapenye dziko; popeza ndakuika cizindikilo ca nyumba ya Israyeli.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 12

Onani Ezekieli 12:6 nkhani