Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 1:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi pamwamba pa thambo linali pamitu pao panali cifaniziro ca mpando wacifumu, maonekedwe ace ngati mwala wa safiro; ndipo pa cifaniziro ca mpando wacifumu panali cifaniziro ngati maonekedwe ace a munthu wokhala pamwamba pace.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 1

Onani Ezekieli 1:26 nkhani