Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 8:22 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti ndinacita manyazi kupempha kwa mfumu gulu la asilikari, ndi apakavalo, kutithandiza pa adani panjira; popeza tidalankhula ndi mfumu kuti, Dzanja la Mulungu wathu likhalira mokoma onse akumfuna; koma mphamvu yace ndi mkwiyo wace zitsutsana nao onse akumsiya.

Werengani mutu wathunthu Ezara 8

Onani Ezara 8:22 nkhani