Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 7:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo iwe Ezara monga mwa nzeru za Mulungu wako iri m'dzanja lako, uike nduna, ndi oweruza mirandu, aweruze anthu onse ali tsidya lija la mtsinje, onse akudziwa malamulo a Mulungu wako; ndi wosawadziwayo umphunzitse.

Werengani mutu wathunthu Ezara 7

Onani Ezara 7:25 nkhani