Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezara 7:24 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Tikudziwitsaninso kuti sikudzaloledwa kusonkhetsa ali yense wa ansembe, ndi Alevi, oyimbira, odikira, Anetini, kapena anchito a nyumba iyi ya Mulungu msonkho, thangata, kapena msonkho wa panjira.

Werengani mutu wathunthu Ezara 7

Onani Ezara 7:24 nkhani